Pakwitana Mbuye Wanga

 


1. Pakwitana Mbuye wanga
Potsiriza dzikoli,
Pakufika tsiku lakuwalalo
Posonkhana akumvera,
Pakuona Yesuyo,
Tidzakondwerera naye komweko.


Refrain
Pakwitana Mbuye wanga,
Pakwitana Mbuye wanga,
Pakwitana Mbuye wanga,
Tidzakondwerera naye komweko.


2. Potuluka m’manda mwawo
Anthu ake onsewo,
Tidzasanganatu naow nthawiyo,
Pakuuka osankhidwa,
Kunka naye Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.


3. Tisaleke kigwirabe
Ntchito ya Mulunguyo,
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli,
Ndi podzatha moyo wathu
Ndi zintchito zathuzo,
Tidzakonddwerera naye komweko.

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *