Tamani Mphamvu

 


1. Tamani mphamvu ya Yesu,
Angelo agwade;
Tulutsani korona,


Ref
Mubveke, mbveke, mbveke,
Mbveke, Mbuyeyo!


2. Inu osankhidwa ake,
Owomboledwa ‘nu,
Tamani Mpulumutsiyo,


3. Anthu ose ndi mitundu
Pa dziko linotu,
Amlemekeze Mfumuyi,


4. Tifuna kuti komweko
Tikamgwadire ‘Ye;
Tidzaimba kosaleka;

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *